Proverbs 17:15 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Woweruza munthu woipa mtima kuti ndi wosalakwa, amanyansa Chauta, nayenso wopasa mlandu munthu wosalakwa amaipira Chauta.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wokometsa mlandu wa wamphulupulu, ndi wotsutsa wolungama, onse awiriwa amnyansa Yehova.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kumasula munthu wolakwa kapena kumanga munthu wosalakwa, zonse ziwirizi Yehova zimamunyansa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wokometsa mlandu wa wamphulupulu, ndi wotsutsa wolungama, Onse awiriwa amnyansa Yehova.