Proverbs 17:2 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kapolo wochita zinthu mwanzeru adzalamula mwana wa mfulu wochita zamanyazi, kapoloyo adzagaŵana nawo choloŵa ngati mmodzi mwa abale.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kapolo wochita mwanzeru adzalamulira mwana wochititsa manyazi, nadzagawana nao abale cholowa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kapolo wanzeru adzalamulira mwana wochititsa manyazi, ndipo kapoloyo adzagawana nawo cholowa ngati mmodzi mwa abale.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kapolo wocitamwanzeru Adzalamulira mwana wocititsa manyazi, Nadzagawana nao abale colowa.