Proverbs 17:22 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mtima wosangalala umakhala ngati mankhwala abwino, koma mtima woziya umaumitsa thupi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mtima wosekerera uchiritsa bwino; koma mzimu wosweka uphwetsa mafupa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mtima wosangalala uli ngati mankhwala abwino, koma mtima wokhumudwa umafowoketsa mafupa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mtima wosekerera uciritsa bwino Koma mzimu wosweka uphwetsa mafupa,