Proverbs 17:24 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthu wanzeru amaika mtima pa nzeru, koma chitsiru chimangoti maso mwalamwala pa dziko lonse.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Nzeru ili pamaso pa wozindikira; koma maso a wopusa ali m'malekezero a dziko.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu wozindikira zinthu, maso ake amakhala pa nzeru, koma chitsiru chimwazamwaza maso ake pa dziko lonse lapansi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Nzeru iri pamaso pa wozindikira; Koma maso a wopusa ali m'malekezero a dziko.