Proverbs 17:25 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mwana wopusa amamvetsa chisoni atate ake, ndipo amapweteka mtima wa amai ake amene adambala.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mwana wopusa achititsa atate wake chisoni, namvetsa zowawa amake wombala.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mwana wopusa amamvetsa chisoni abambo ake ndipo amapweteketsa mtima amayi ake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mwana wopusa acititsa atate wace cisoni, Namvetsa zowawa amace wombala.