Proverbs 17:27 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthu wosunga pakamwa ndiye wodziŵa zinthu, munthu wodekha mtima ndiye womvetsa zinthu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wopanda chikamwakamwa apambana kudziwa; ndipo wofatsa mtima ali wanzeru.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu wosunga pakamwa ndiye wodziwa zinthu, ndipo wodekha mtima ndiye womvetsa bwino zinthu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wopanda cikamwakamwa apambana kudziwa; Ndipo wofatsa mtima ali wanzeru.