Proverbs 18:11 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chuma cha munthu wolemera chili ngati mzinda wake wolimba, chili ngati linga lalitali limene amayesa ndi lomutchinjiriza.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Chuma cha wolemera ndicho mudzi wake wolimba; alingalira kuti ndicho khoma lalitali.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Chuma cha anthu olemera chili ngati mzinda wake wolimba; chili ngati khoma lalitali limene amaganiza kuti limutchinjiriza.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Cuma ca wolemera ndico mudzi wace wolimba; Alingalira kuti ndico khoma lalitari.