Proverbs 18:12 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chiwonongeko chisanafike, mtima wa munthu umadzikuza, koma ulemu umatsatira kudzichepetsa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mtima wa munthu unyada asanaonongeke; koma chifatso chitsogolera ulemu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Chiwonongeko chisanafike, mtima wa munthu umakhala wonyada, koma ulemu umatsatira kudzichepetsa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mtima wa munthu unyada asanaonongeke; Koma cifatso citsogolera ulemu.