Proverbs 18:14 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mtima wa munthu umatha kupirira matenda, koma munthu akataya mtima, ndani angathe kumlimbitsanso?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mtima wa munthu umlimbitsa alikudwala; koma ndani angatukule mtima wosweka?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mtima wa munthu utha kupirira pa matenda, koma munthu akataya mtima ndani angathe kumulimbitsanso.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mtima wa munthu umlimbitsa alikudwala; Koma ndani angatukule mtima wosweka?