Proverbs 18:15 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthu wochenjera amafuna kuphunzirabe zambiri, amafunitsitsa kudziŵa bwino zinthu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mtima wa wozindikira umaphunzira; khutu la anzeru lifunitsa kudziwa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu wanzeru amawonjezera nzeru zina; amafunafuna kudziwa bwino zinthu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mtima wa wozindikira umaphunzira; Khutu la anzeru lifunitsa kudziwa.