Proverbs 18:16 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mphatso ya munthu imakhala ngati konza kapansi, imatha kumfikitsa pamaso pa akuluakulu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mtulo wa munthu umtsegulira njira, numfikitsa pamaso pa akulu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mphatso ya munthu imamutsekulira njira yomufikitsa pamaso pa anthu akuluakulu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mtulo wa munthu umtsegulira njira, Numfikitsa pamaso pa akuru.