Proverbs 18:17 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Amene amayamba kufotokoza mlandu wake amaoneka ngati wokhoza ndiye, mpaka mnzake atabwera nadzamufunsitsa bwino.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Woyamba kudzinenera ayang'anika wolungama; koma mnzake afika namuululitsa zake zonse.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Amene amayamba kufotokoza mlandu wake amaoneka ngati wolungama ndiye mpaka mnzake atabwera ndi kumufunsa bwino.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Woyamba kudzinenera ayang'anika wolungama; Koma mnzace afika namuululitsa zace zonse.