Proverbs 18:19 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mnzako ukamthandiza amakhala ngati mzinda wolimba, koma kukangana naye kumakutsekera thandizo lililonse.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kupembedza mbale utamchimwira nkovuta, kulanda mudzi wolimba nkosavuta; makangano akunga mipiringidzo ya linga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mʼbale amene wamuthandiza amakhala ngati mzinda wolimba, koma kukangana naye kumatsekereza thandizo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kupembedza mbale utamcimwira nkobvuta, Kulanda mudzi wolimba nkosabvuta; Makangano akunga mipiringidzo ya linga.