Proverbs 18:3 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kuipa mtima kukaoneka, pamabweranso manyozo, kunyozeka kumaitana manyazi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakudza wamphulupulu padzanso kunyoza; manyazi natsagana ndi chitonzo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kuyipa mtima kukabwera, manyozonso amabwera. Manyazi amabwera pamodzi ndi kunyozeka.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakudza wamphulupulu padzanso kunyoza; Manyazi natsagana ndi citonzo.