Proverbs 18:4 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mau a munthu angathe kukhala kasupe wa nzeru, ozama ngati nyanja yamchere yaikulu, omweka ngati a mu mtsinje wothamanga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mau a m'kamwa mwa munthu ndiwo madzi akuya; kasupe wa nzeru ndiye mtsinje wodzala.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mawu a munthu ali ngati madzi akuya, kasupe wa nzeru ndiye mtsinje wotumphuka.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mau a m'kamwa mwa munthu ndiwo madzi akuya; Kasupe wa nzeru ndiye mtsinje wodzala.