Proverbs 18:8 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mau a kazitape ali ngati chakudya chokoma, anthu amaŵameza onse mokondwa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mau akazitape akunga zakudya zolongosoka, zotsikira m'kati mwa mimba.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mawu a miseche ali ngati chakudya chokoma; amalowa mʼmimba mwa munthu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mau a kazitape akunga zakudya zolongosoka, Zotsikira m'kati mwa mimba.