Proverbs 18:9 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Wogwira ntchito yake mwaulesi, ali pachibale ndi munthu woononga zinthu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wogwira ntchito mwaulesi ndiye mbale wake wa wosakaza.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu waulesi pa ntchito yake ali pachibale ndi munthu amene amawononga zinthu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wogwira nchito mwaulesi Ndiye mbale wace wa wosakaza.