Proverbs 19:10 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nkosayenera kuti chitsiru chizikhala ndi moyo wachuma, nanjinso kuti kapolo azilamulira akalonga!
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wopusa sayenera kukhala ndi zinthu zolongosoka; nanga kapolo ayenera kulamulira akalonga kodi?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Nʼkosayenera kuti chitsiru chizikhala ndi moyo wamanyado, nanjinso kuti kapolo azilamulira akalonga!
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wopusa sayenera kukhala ndi zinthu zolongosoka; Nanga kapolo ayenera kulamulira akalonga kodi?