Proverbs 19:12 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mkwiyo wa mfumu uli ngati kubangula kwa mkango, koma kukoma mtima kwake kuli ngati mame pa udzu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mkwiyo wa mfumu ukunga kubangula kwa mkango; koma kukoma mtima kwake kunga mame pamsipu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mkwiyo wa mfumu uli ngati kubangula kwa mkango, koma kukoma mtima kwake kuli ngati mame pa udzu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mkwiyo wa mfumu ukunga kubangula kwa mkango; Koma kukoma mtima kwace kunga mame pamsipu.