Proverbs 19:13 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mwana wopusa ndi tsoka kwa atate ake, mkazi wolongolola ndi wotopetsa ngati mvula ya mvumbi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mwana wopusa ndiye tsoka la atate wake; ndipo makangano a mkazi ndiwo kudonthadonthabe.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mwana wopusa ndiye tsoka la abambo ake ndipo mkazi wolongolola ndi wotopetsa ngati mvula yamvumbi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mwana wopusa ndiye tsoka la atate wace; Ndipo makangano a mkazi ndiwo kudontha-donthabe.