Proverbs 19:14 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nyumba ndi chuma ndiye choloŵa chochokera kwa makolo, koma mkazi wanzeru ndi wochokera kwa Chauta.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Nyumba ndi chuma ndizo cholowa cha atate; koma mkazi wanzeru achokera kwa Yehova.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Nyumba ndi chuma ndiye cholowa chochokera kwa makolo; koma mkazi wanzeru ndi wochokera kwa Yehova.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Nyumba ndi cuma ndizo colowa ca atate; Koma mkazi wanzeru acokera kwa Yehova.