Proverbs 19:17 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Wokomera mtima anthu osauka amachita ngati wokongoza Chauta, ndipo ndi Chautayo amene adzambwezera chifukwa cha ntchito zake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wochitira waumphawi chifundo abwereka Yehova; adzambwezera chokoma chakecho.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Amene amakomera mtima osauka amachita ngati wakongoletsa Yehova, ndipo Yehovayo ndiye adzamubwezere.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wocitira waumphawi cifundo abwereka Yehova; Adzambwezera cokoma caceco.