Proverbs 19:2 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Si bwino kuti munthu akhale wosadziŵa zinthu, ndipo munthu woyenda mofulumira dziŵi amasokera.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kukhumba kosadziwa sikuli kwabwino; ndipo wofulumira ndi mapazi ake amachimwa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Si bwino kuti munthu akhale wopanda nzeru; ndipo munthu woyenda mofulumira amaphonya njira.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kukhumba kosadziwa sikuli kwabwino; Ndipo wofulumira ndi mapazi ace amacimwa.