Proverbs 19:21 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthu mumtima mwake amakonzekera zambiri, koma cholinga cha Chauta ndiye chimene chidzachitike.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Muli zolingalira zambiri m'mtima mwa munthu; koma uphungu wa Yehova ndiwo udzaimika.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu amakonzekera zambiri mu mtima mwake, koma cholinga cha Yehova ndiye chidzachitike.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Muli zolingalira zambiri m'mtima mwa munthu; Koma uphungu wa Yehova ndiwo udzaimika.