Proverbs 19:22 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chofunika kwa munthu nkukhulupirika. Kukhala wosauka nkwabwino koposa kukhala wonama.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Chotikondetsa munthu ndicho kukoma mtima kwake; ndipo wosauka apambana munthu wonama.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Chimene munthu amafuna ndi chikondi chosatha; nʼkwabwino kukhala wosauka kusiyana ndi kukhala wabodza.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Cotikondetsa munthu ndico kukoma mtima kwace; Ndipo wosauka apambana munthu wonama.