Proverbs 19:24 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Waulesi amati akapisa dzanja m'mbale, kumamtopetsa kuti alifikitse kukamwa kwake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Waulesi alonga dzanja lake m'mbale, osalibwezanso kukamwa kwake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu waulesi amapisa dzanja lake mʼmbale; koma sangathe kufikitsa dzanja lakelo pakamwa pake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wolesi alonga dzanja lace m'mbale, Osalibwezanso kukamwa kwace.