Proverbs 19:26 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Amene amachita ndeu ndi atate ake ndi kupirikitsa amai ake, ameneyo ndi mwana wochititsa manyazi ndiponso wonyozetsa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wolanda za atate, ndi wopirikitsa amai, ndiye mwana wochititsa manyazi ndi wogwetsa nkhope.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mwana wochita ndewu ndi abambo ake ndi kuthamangitsa amayi ake, ndi mwana wochititsa manyazi ndi wonyozetsa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wolanda za atate, ndi wopitikitsa amai, Ndiye mwana wocititsa manyazi ndi wogwetsa nkhope.