Proverbs 19:27 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mwana wanga, ukaleka kumvera malangizo, udzapatukana ndi mau opatsa nzeru.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ukangofuna, mwananga, kusochera kusiya mau akudziwitsa, leka kumva mwambo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mwana wanga, ukaleka kumvera malangizo, udzapatukana ndi mawu opatsa nzeru.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ukangofuna, mwananga, kusocera kusiya mau akudziwitsa, Leka kumva mwambo.