Proverbs 19:29 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Zakonzeka kale kuti mlandu uŵagwere anthu onyoza, mkwapulo ndi wokonzakonza kuti akwapulire pamsana pa zitsiru.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Akonzera onyoza chiweruzo, ndi mikwingwirima pamsana pa opusa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Chilango chakonzedwa kale kuti chigwere anthu oyipa, ndipo mkwapulo wakonzedwa kale kuti ukwapule misana ya anthu opusa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Akonzera onyoza ciweruzo, Ndi mikwingwirima pamsana pa opusa.