Proverbs 19:6 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ambiri amafuna kuti munthu wopata aŵakomere mtima, munthu wooloŵa manja amakhala bwenzi la anthu onse.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ambiri adzapembedza waufulu; ndipo yense ndi bwenzi la munthu wopatsa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anthu ambiri amafuna munthu wopatsa kuti awakomere mtima, ndipo munthu amene amapereka mphatso ndi bwenzi la munthu aliyense.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ambiri adzapembedza waufulu; Ndipo yense ndi bwenzi la munthu wopatsa.