Proverbs 19:7 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ngati munthu wosauka abale ake omwe amadana naye, nanji abwenzi ake tsono! Iwo ndiye adzamthaŵira kunka kutali. Amayesetsa kuŵalondola mopembedzera, koma osaŵathanso.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Abale onse a wosauka amuda; nanga mabwenzi ake kodi satanimphirana naye? Awatsata ndi mau, koma kuli zii.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ngati munthu wosauka abale ake omwe amadana naye, nanji abwenzi ake tsono! Iwo adzamuthawa kupita kutali. Amayesa kuwatsatira mowapembedza koma iwo samapezeka konse.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Abale onse a wosauka amuda; Nanga mabwenzi ace kodi satanimphirana naye? Awatsata ndi mau, koma kuli zi.