Proverbs 2:17 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
amene amasiya mwamuna wake wapaumbeta, kuiŵala chipangano chochita ndi Mulungu wake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
wosiya bwenzi la ubwana wake, naiwala chipangano cha Mulungu wake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
amene wasiya mwamuna wa chitsikana wake ndi kuyiwala pangano limene anachita pamaso pa Mulungu wake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wosiya bwenzi la ubwana wace, Naiwala cipangano ca Mulungu wace;