Proverbs 20:27 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mpweya wa munthu uli ngati nyale ya Chauta, nyaleyo imafufuza ziwalo zake zonse zam'kati.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mzimu wa munthu ndiwo nyali ya Yehova; usanthula m'kati monse mwa mimba.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mpweya wa munthu uli ngati nyale ya Yehova; imafufuza ziwalo zake zonse zamʼkati.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mzimu wa munthu ndiwo nyali ya Yehova; Usanthula m'kati monse mwa mimba.