Proverbs 20:9 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndani angathe kunena kuti, “Ine ndauyeretsa mtima wanga, ndilibenso tchimo lililonse.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndani anganene, Ndasambitsa mtima wanga, ndayera opanda tchimo?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndani amene anganene kuti, “Ndawuyeretsa mtima wanga; ndilibe tchimo lililonse?”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndani anganene, Ndasambitsa mtima wanga, Ndayera opanda cimo?