Proverbs 21:1 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mtima wa mfumu uli ngati mtsinje wa madzi m'manja mwa Chauta. Amauwongolera ku zimene Iyeyo akufuna.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mtima wa mfumu uli m'dzanja la Yehova ngati mitsinje ya madzi; aulozetsa komwe afuna.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mtima wa mfumu uli ngati mtsinje wamadzi mʼdzanja la Yehova; Iye amautsongolera pa chilichonse chimene akufuna.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mtima wa mfumu uli m'dzanja la Yehova ngati mitsinje ya madzi; Aulozetsa komwe afuna.