Proverbs 21:10 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mtima wa munthu woipa umalakalaka zoipa. Samva chifundo konse ndi mnzake wovutika.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wamphulupulu mtima wake umkhumba zoipa; sakomera mtima mnzake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu woyipa amalakalaka zoyipa; sachitira chifundo mnansi wake wovutika.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wamphulupulu mtima wace umkhumba zoipa; Sakomera mtima mnzace.