Proverbs 21:16 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthu amene amasiya njira ya anthu anzeru, adzapezeka m'gulu la anthu akufa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Munthu wosochera pa njira ya nzeru adzakhala m'msonkhano wa akufa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu amene amachoka pa njira ya anthu anzeru adzapezeka mʼgulu la anthu akufa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Munthu wosocera pa njira ya nzeru Adzakhala m'msonkhano wa akufa.