Proverbs 21:19 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kuli bwino kukhala ku chipululu kupambana kukhala ndi mkazi wolongolola ndi wopsa mtima msanga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kukhala m'chipululu kufunika kuposa kukhala ndi mkazi wolongolola ndi wong'ung'udza.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Nʼkwabwino kukhala mʼchipululu kuposa kukhala ndi mkazi wolongolola ndi wopsa mtima msanga.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kukhala m'cipululu kufunika Kuposa kukhala ndi mkazi wolongolola ndi wong'ung'udza.