Proverbs 21:20 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthu wanzeru samwaza chuma chake, koma munthu wopusa amachiwononga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mokhala wanzeru muli katundu wofunika ndi mafuta; koma wopusa angozimeza.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu wanzeru samwaza chuma chake, koma wopusa amachiwononga.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mokhala wanzeru muli katundu wofunika ndi mafuta; Koma wopusa angozimeza.