Proverbs 21:22 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthu wanzeru amagonjetsa mzinda wa anthu a mphamvu, ndipo amagwetsa linga lamphamvu limene anthuwo ankalikhulupirira.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wanzeru akwera pa mudzi wa olimba, nagwetsa mphamvu yake imene anaikhulupirira.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu wanzeru amagonjetsa mzinda wa anthu amphamvu ndi kugwetsa linga limene iwo amalidalira.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wanzeru akwera pa mudzi wa olimba, Nagwetsa mphamvu yace imene anaikhulupirira.