Proverbs 21:24 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthu wonyada ndi wodzikuza amamtchula “Mnyodoli,” chifukwa amachita zinthu modzitama ndi mwachipongwe.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wonyada wodzikuza dzina lake ndiye wonyoza; achita mwaukali modzitama.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu wonyada ndi wodzikuza amamutcha, “Mnyodoli,” iye amachita zinthu modzitama kwambiri.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wonyada wodzikuza dzina lace ndiye wonyoza; Acita mwaukali modzitama.