Proverbs 21:25 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kulakalaka kwa munthu waulesi kumamupha, poti amangokhala manja ali khoba, osagwira ntchito.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Chifuniro cha waulesi chimupha; chifukwa manja ake akana kugwira ntchito.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Chilakolako cha munthu waulesi chidzamupha yekha chifukwa manja ake amangokhala goba osagwira ntchito.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Cifuniro ca wolesi cimupha; Cifukwa manja ace akana kugwira nchito.