Proverbs 21:26 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsiku lathunthu anthu oipa amasirira zinthu, koma omvera Mulungu amapatsa ndipo alibe kaliwumira.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ena asirira modukidwa tsiku lonse; koma wolungama amapatsa osamana.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tsiku lonse anthu oyipa amasirira zambiri, koma anthu olungama amapereka mowolowamanja.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ena asirira modukidwa tsiku lonse; Koma wolungama amapatsa osamana.