Proverbs 21:27 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nsembe ya anthu oipa imamnyansa Chauta, nanji tsono akaipereka ndi cholinga choipa!
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Nsembe ya oipa inyansa; makamaka pakudza nayo iwo mwachiwembu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Nsembe ya anthu oyipa imamunyansa Yehova, nanji akayipereka ndi cholinga choyipa!
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Nsembe ya oipa inyansa; Makamaka pakudza nayo iwo mwaciwembu.