Proverbs 21:28 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mboni yonama idzaonongeka, koma mau a munthu wakumva adzamveka nthaŵi zonse.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mboni yonama idzafa; koma mwamuna wakumvetsa adzanena mosakayika.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mboni yonama idzawonongeka, koma mawu a munthu wakumva adzakhala nthawi zonse.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mboni yonama idzafa; Koma mwamuna wakumvetsa adzanena mosakayika,