Proverbs 21:29 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthu woipa amafuna kuwoneka wolimba mtima, koma munthu woongoka amaganizira bwino zochita zake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Munthu woipa aumitsa nkhope yake; koma woongoka mtima akonza njira zake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu woyipa amafuna kudzionetsa ngati wolimba mtima, koma munthu wowongoka amaganizira njira zake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Munthu woipa aumitsa nkhope yace; Koma woongoka mtima akonza njira zace.