Proverbs 21:31 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kavalo amamkonzera tsiku la nkhondo, koma ndi Chauta amene amapambanitsa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kavalo amakonzedweratu chifukwa cha tsiku la nkhondo; koma wopulumutsa ndiye Yehova.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kavalo amamukonzera tsiku la nkhondo, koma ndi Yehova amene amapambanitsa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kavalo amakonzedweratu cifukwa ca tsiku la nkhondo; Koma wopulumutsa ndiye Yehova.