Proverbs 21:4 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Maso odzikuza ndi mtima wonyada zimatsogolera anthu oipa ngati nyale, nchifukwa chake amachimwa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Maso akunyada, ndi mtima wodzikuza, ndi nyali ya oipa, zili tchimo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Maso odzikuza ndi mtima wonyada, zimatsogolera anthu oyipa ngati nyale nʼchifukwa chake amachimwa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Maso akunyada, ndi mtima wodzikuza, Ndi nyali ya oipa, ziri cimo.