Proverbs 21:7 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndeu za anthu oipa zidzaŵaononga, poti amakana kuchita zolungama.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Chiwawa cha amphulupulu chidzawakokolola; chifukwa akana kuchita chiweruzo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Chiwawa cha anthu oyipa chidzawawononga, pakuti iwo amakana kuchita zolungama.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ciwawa ca amphulupulu cidzawakokolola; Cifukwa akana kucita ciweruzo.