Proverbs 21:8 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Njira ya munthu woipa ndi yokhotakhota, koma khalidwe la munthu wosachimwa ndi lolungama.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wosenza tchimo njira yake ikhotakhota; koma ntchito ya woyera mtima ilungama.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Njira ya munthu wolakwa ndi yokhotakhota, koma makhalidwe a munthu wosalakwa ndi olungama.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wosenza cimo njira yace ikhotakhota; Koma nchito ya woyera mtima ilungama.